Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 1018 Yesu afuna iwe unnke kwawoko,
Yesu afuna iwe unnke kwawoko,
Lowa m’njira yake yakuyerayeratu;
Anadzera m’Mwamba kutiperekezako;
Yamba msanga iwe kunka kwanuko.
Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 1018 Yesu afuna iwe unnke kwawoko,
Yesu afuna iwe unnke kwawoko,
Lowa m’njira yake yakuyerayeratu;
Anadzera m’Mwamba kutiperekezako;
Yamba msanga iwe kunka kwanuko.